Mitu

  1. 1
  2. 2
  3. 3
  4. 4
  5. 5
  6. 6
  7. 7
  8. 8
  9. 9
  10. 10
  11. 11
  12. 12
  13. 13
  14. 14
  15. 15
  16. 16
  17. 17
  18. 18
  19. 19
  20. 20
  21. 21
  22. 22
  23. 23
  24. 24
  25. 25
  26. 26
  27. 27
  28. 28
  29. 29
  30. 30
  31. 31
  32. 32
  33. 33
  34. 34
  35. 35
  36. 36
  37. 37
  38. 38
  39. 39
  40. 40
  41. 41
  42. 42
  43. 43
  44. 44
  45. 45
  46. 46
  47. 47
  48. 48
  49. 49
  50. 50
  51. 51
  52. 52
  53. 53
  54. 54
  55. 55
  56. 56
  57. 57
  58. 58
  59. 59
  60. 60
  61. 61
  62. 62
  63. 63
  64. 64
  65. 65
  66. 66
  67. 67
  68. 68
  69. 69
  70. 70
  71. 71
  72. 72
  73. 73
  74. 74
  75. 75
  76. 76
  77. 77
  78. 78
  79. 79
  80. 80
  81. 81
  82. 82
  83. 83
  84. 84
  85. 85
  86. 86
  87. 87
  88. 88
  89. 89
  90. 90
  91. 91
  92. 92
  93. 93
  94. 94
  95. 95
  96. 96
  97. 97
  98. 98
  99. 99
  100. 100
  101. 101
  102. 102
  103. 103
  104. 104
  105. 105
  106. 106
  107. 107
  108. 108
  109. 109
  110. 110
  111. 111
  112. 112
  113. 113
  114. 114
  115. 115
  116. 116
  117. 117
  118. 118
  119. 119
  120. 120
  121. 121
  122. 122
  123. 123
  124. 124
  125. 125
  126. 126
  127. 127
  128. 128
  129. 129
  130. 130
  131. 131
  132. 132
  133. 133
  134. 134
  135. 135
  136. 136
  137. 137
  138. 138
  139. 139
  140. 140
  141. 141
  142. 142
  143. 143
  144. 144
  145. 145
  146. 146
  147. 147
  148. 148
  149. 149
  150. 150

Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Davide ayimbira ulemerero wa Mulungu, ndi ulemu umene Mulungu acitira mtundu wa anthu

Kwa Mkulu wa Nyimbo; pa Oititl. Salnto la Davide.

1. Yehova, Ambuye wathu,Dzina lanu liposadi nanga pa dziko lonse lapansi!Inu amene munaika ulemerero wanu pa thambo la kumwamba.

2. M'kamwa mwa makanda ndi oyamwamunakhazikitsamphamvu,Cifukwa ca otsutsana ndi Inu,Kuti muwaletse mdani ndi wobwezera cilango.

3. Pakuona ine thambo la kumwamba lanu, nchito ya zala zanu,Mwezi ndi nyenyezi, zimene munazikhazika,

4. Munthu ndani kuti mumkumbukila?Ndi mwana wa munthu kuti muceza naye?

5. Pakuti munamcepsa pang'ono ndi Mulungu,Munambveka iye korona wa ulemerero ndi ulemu.

6. Munamcititsa ufumu pa nchito za manja anu;Mudagonjetsa zonse pansi pa mapazi ace;

7. Nkhosa ndi ng'ombe, zonsezo,Ndi nyama za kuthengo zomwe;

8. Mbalame za m'mlengalenga, ndi nsomba za m'nyanja.Zopita m'njira za m'nyanja.

9. Yehova, Ambuye wathu,Dzina lanu liposadi nanga pa dziko lonse lapansi!