Mitu

  1. 1
  2. 2
  3. 3
  4. 4
  5. 5
  6. 6
  7. 7
  8. 8
  9. 9
  10. 10
  11. 11
  12. 12
  13. 13
  14. 14
  15. 15
  16. 16
  17. 17
  18. 18
  19. 19
  20. 20
  21. 21
  22. 22
  23. 23
  24. 24
  25. 25
  26. 26
  27. 27
  28. 28
  29. 29
  30. 30
  31. 31
  32. 32
  33. 33
  34. 34
  35. 35
  36. 36
  37. 37
  38. 38
  39. 39
  40. 40
  41. 41
  42. 42
  43. 43
  44. 44
  45. 45
  46. 46
  47. 47
  48. 48
  49. 49
  50. 50
  51. 51
  52. 52
  53. 53
  54. 54
  55. 55
  56. 56
  57. 57
  58. 58
  59. 59
  60. 60
  61. 61
  62. 62
  63. 63
  64. 64
  65. 65
  66. 66
  67. 67
  68. 68
  69. 69
  70. 70
  71. 71
  72. 72
  73. 73
  74. 74
  75. 75
  76. 76
  77. 77
  78. 78
  79. 79
  80. 80
  81. 81
  82. 82
  83. 83
  84. 84
  85. 85
  86. 86
  87. 87
  88. 88
  89. 89
  90. 90
  91. 91
  92. 92
  93. 93
  94. 94
  95. 95
  96. 96
  97. 97
  98. 98
  99. 99
  100. 100
  101. 101
  102. 102
  103. 103
  104. 104
  105. 105
  106. 106
  107. 107
  108. 108
  109. 109
  110. 110
  111. 111
  112. 112
  113. 113
  114. 114
  115. 115
  116. 116
  117. 117
  118. 118
  119. 119
  120. 120
  121. 121
  122. 122
  123. 123
  124. 124
  125. 125
  126. 126
  127. 127
  128. 128
  129. 129
  130. 130
  131. 131
  132. 132
  133. 133
  134. 134
  135. 135
  136. 136
  137. 137
  138. 138
  139. 139
  140. 140
  141. 141
  142. 142
  143. 143
  144. 144
  145. 145
  146. 146
  147. 147
  148. 148
  149. 149
  150. 150

Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 132 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Davide asamalira kacisi ndi likasa. Lonjezano la Mulungu

Nyimbo yokwerera.

1. Yehova, kumbukilani Davide Kuzunzika kwace konse;

2. Kuti analumbira Yehova,Nawindira Wamphamvuyo wa Yakobo, ndi kuti,

3. Ngati ndidzalowa pakhomo pa nyumba yanga,Ngati ndidzakwera pa kama logonapo;

4. Ngati ndidzalola maso anga agone,Kapena zikope zanga ziodzere;

5. Kufikira nditapezera Yehova malo,Cokhalamo Wamphamvuyo wa Yakobo?

6. Taonani, tinacimva m'Efrata;Tinacipeza ku cidikha ca kunkhalango.

7. Tidzalowa mokhalamo Iye;Tidzagwadira ku mpando wa mapazi ace.

8. Ukani, Yehova, lowani ku mpumulo wanu;Inu ndi hema wa mphamvu yanu,

9. Ansembe anu abvale cilungamo;Ndi okondedwa anu apfuule mokondwera.

10. Cifukwa ca Davide mtumiki wanuMusabweze nkhope ya wodzozedwa wanu.

11. Yehova analumbira Davide zoona;Sadzalibweza; ndi kuti,Wa iwo okhala zipatso za thupi lako ndidzaika pa mpando wacifumu wako.

12. Ana ako akasunga cipangano cangaNdi mboni yanga imene ndidzawaphunzitsa,Ana aonso adzakhala pa mpando wanu ku nthawi zonse,

13. Pakuti Yehova anasankha Ziyoni;Analikhumba likhale pokhala pace; ndi kuti,

14. Pampumulo panga mpano posatha:Pano ndidzakhala; pakuti ndakhumbapo.

15. Ndidzadalitsatu cakudya cace;Aumphawi ace ndidzawakhutitsa ndi mkate.

16. Ndipo ansembe ace ndidzawabveka ndi cipulumutso:Ndi okondedwa ace adzapfuulitsa mokondwera.

17. Apo ndidzaphukitsira Davide nyanga;Ndak onzeraru wodzozedwa wanga nyali.

18. Ndidzawabvekaadani ace ndi manyaziKoma pa iyeyu korona wace adzambveka.