Mitu

  1. 1
  2. 2
  3. 3
  4. 4
  5. 5
  6. 6
  7. 7
  8. 8
  9. 9
  10. 10
  11. 11
  12. 12
  13. 13
  14. 14
  15. 15
  16. 16
  17. 17
  18. 18
  19. 19
  20. 20
  21. 21
  22. 22
  23. 23
  24. 24
  25. 25
  26. 26
  27. 27
  28. 28
  29. 29
  30. 30
  31. 31
  32. 32
  33. 33
  34. 34
  35. 35
  36. 36
  37. 37
  38. 38
  39. 39
  40. 40
  41. 41
  42. 42
  43. 43
  44. 44
  45. 45
  46. 46
  47. 47
  48. 48
  49. 49
  50. 50
  51. 51
  52. 52
  53. 53
  54. 54
  55. 55
  56. 56
  57. 57
  58. 58
  59. 59
  60. 60
  61. 61
  62. 62
  63. 63
  64. 64
  65. 65
  66. 66
  67. 67
  68. 68
  69. 69
  70. 70
  71. 71
  72. 72
  73. 73
  74. 74
  75. 75
  76. 76
  77. 77
  78. 78
  79. 79
  80. 80
  81. 81
  82. 82
  83. 83
  84. 84
  85. 85
  86. 86
  87. 87
  88. 88
  89. 89
  90. 90
  91. 91
  92. 92
  93. 93
  94. 94
  95. 95
  96. 96
  97. 97
  98. 98
  99. 99
  100. 100
  101. 101
  102. 102
  103. 103
  104. 104
  105. 105
  106. 106
  107. 107
  108. 108
  109. 109
  110. 110
  111. 111
  112. 112
  113. 113
  114. 114
  115. 115
  116. 116
  117. 117
  118. 118
  119. 119
  120. 120
  121. 121
  122. 122
  123. 123
  124. 124
  125. 125
  126. 126
  127. 127
  128. 128
  129. 129
  130. 130
  131. 131
  132. 132
  133. 133
  134. 134
  135. 135
  136. 136
  137. 137
  138. 138
  139. 139
  140. 140
  141. 141
  142. 142
  143. 143
  144. 144
  145. 145
  146. 146
  147. 147
  148. 148
  149. 149
  150. 150

Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 66 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Acenjeza onse alemekeze Mulungu pa nchito zace zodabwiza

Kwa Mkulu wa Nyimbo. Nyimbo. Salmo.

1. Pfuulirani kwa Mulungu, dziko lonse lapansi.

2. Yimbirani ulemerero wa dzina lace;Pomlemekeza mumcitire ulemerero.

3. Nenani kwa Mulungu, Ha, nchito zanu nzoopsa nanga!Cifukwa ca mphamvu yanu yaikuru adani anu adzagonjera Inu,

4. Dziko lonse lapansi lidzakugwadirani,Ndipo lidzakuyimbirani;Adzayimbira dzina lanu.

5. Idzani, muone nchito za Mulungu;Zocitira Iye ana a anthu nzoopsa.

6. Anasanduliza nyanja ikhale mtunda:Anaoloka mtsinje coponda pansi:Apo tinakondwera mwa Iye.

7. Acita ufumu mwa mphamvu yace kosatha;Maso ace ayang'anira amitundu;Opikisana ndi Iye asadzikuze.

8. Lemekezani Mulungu wathu, mitundu ya anthu inu,Ndipo mumveketse liu la cilemekezo cace:

9. Iye amene asunga moyo wathu tingafe,Osalola phazi lathu literereke.

10. Pakati munatiyesera, Mulungu:Munatiyenga monga ayenga siliya.

11. Munapita nafe kuukonde;Munatisenza cothodwetsa pamsana pathu.

12. Munapititsa anthu oberekeka pamwamba pamitu pathu;Tinapyola moto ndi madzi; Koma munatifikitsa potitsitsimutsa.

13. Ndidzalowa m'nyumba yanu ndi nsembe zopsereza,Ndidzakucitirani zowinda zanga,

14. Zimene inazichula milomo yanga,Ndinazinena pakamwa panga pasautsika ine.

15. Ndidzakufukizirani nsembe zapsereza zonona,Pamodzi ndi cofukiza ca mphongo za nkhosa;Ndidzakonza ng'ombe pamodzi ndi mbuzi.

16. Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu,Ndipo ndidzafotokozera zonse anazicitira moyo wanga,

17. Ndinampfuulira Iye pakamwa panga,Ndipo ndinamkuza ndi lilime langa,

18. Ndikadasekera zopanda pace m'mtima mwanga,Ambuye sakadamvera:

19. Koma Mulungu anamvadi; Anamvera mau a pemphero langa,

20. Wolemekezeka Mulungu,Amene sanandipatutsira ine pemphero langa, kapena cifundo cace.