Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 18:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. ndipo popeza anali wa nchito imodzimodzi, anakhala nao, ndipo iwowa anagwira nchito; pakuti nchito yao inali yakusoka mahema.

4. Ndipo anafotokozera m'sunagogemasabata onse, nakopa Ayuda ndi Ahelene.

5. Koma pamene Sila ndi Timoteo anadza potsika ku Makedoniya, Paulo anapsinjidwa ndi mau, nacitira umboni kwa Ayuda kuti Yesu ndiye Kristu.

6. Koma pamene iwo anamkana, nacita mwano, anakutumula maraya ace, nati kwa iwo, Mwazi wanu ukhale pa mitu yanu; ine ndiribe kanthu; kuyambira tsopano ndinka kwa amitundu.

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 18