Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Macitidwe 18:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapeza Myuda wina dzina lace Akula, pfuko lace la ku Ponto, atacoka catsopano ku Italiya, pamodzi ndi mkazi wace Priskila, cifukwa Klaudiyo analamulira Ayuda onse acoke m'Roma; ndipo Pauloanadza kwa iwo:

Werengani mutu wathunthu Macitidwe 18

Onani Macitidwe 18:2 nkhani