Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 13:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndingakhale ndikhoza kunenera, ndipo ndingadziwe zinsinsi zonse, ndi nzeru zonse, ndipo ndingakhale ndiri naco cikhulupiriro conse, kuti ndikasendeza mapiri, koma ndiribe cikondi, ndiri cabe.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 13

Onani 1 Akorinto 13:2 nkhani