Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Akorinto 13:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndingakhale ndilankhula malilime a anthu, ndi a angelo, koma ndiribe cikondi, ndikhala mkuwa woomba, kapena nguli yolira.

Werengani mutu wathunthu 1 Akorinto 13

Onani 1 Akorinto 13:1 nkhani