Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 48:33 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kusekera ndi kukondwa kwacotsedwa, ku munda wobala ndi ku dziko la Moabu; ndipo ndaletsa vinyo pa zoponderamo; sadzaponda ndi kupfuula; kupfuula sikudzakhala kupfuula.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 48

Onani Yeremiya 48:33 nkhani