Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yeremiya 48:32 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwe mpesa wa Sibima; ndidzakulirira iwe ndi kulira kopambana kulira kwa Yazeri, nthambi zako zinapitirira nyanja, zinafikira ku nyanja ya Yazeri; wakufunkha wagwera zipatso zako za mpakasa ndi mphesa zako.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 48

Onani Yeremiya 48:32 nkhani