Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ezekieli 37:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinapenya, taonani, panali mitsempha pa iwo, panadzaponso mnofu, ndi khungu linawakuta pamwamba pace; koma munalibe mpweya mwa iwo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 37

Onani Ezekieli 37:8 nkhani