Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 12:2-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Muononge konse malo onse, amitundu amene mudzawalanda anatumikirako milungu yao, pa mapiri atali, ndi pa zitunda, ndi pansi pa mitengo yonse yabiriwiri;

3. nimugumule maguwa ao a nsembe, ndi kuphwanya zoimiritsa zao, ndi kutentha zifanizo zao, ndi kulikha mafano osema a milungu yao; ndipo muononge dzina lao licoke m'malomo.

4. Musamatero ndi Yehova Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 12