Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 12:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Muononge konse malo onse, amitundu amene mudzawalanda anatumikirako milungu yao, pa mapiri atali, ndi pa zitunda, ndi pansi pa mitengo yonse yabiriwiri;

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 12

Onani Deuteronomo 12:2 nkhani