Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Deuteronomo 12:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Awa ndi malemba ndi maweruzo, muziwasamalirawa kuwacita m'dziko limene Yehova Mulungu wa makolo anu anakupatsani likhale lanu lanu, masiku onse akukhala ndi moyo inu pa dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Deuteronomo 12

Onani Deuteronomo 12:1 nkhani