Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 2:4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu Ayuda anabwera namdzoza Davide pomwepo akhale mfumu ya nyumba ya Yuda.Ndipo wina anauza Davide kuti, Anthu a ku Jabezi Gileadi ndiwo amene anamuika Sauli.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:4 nkhani