Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 2:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pamenepo Davide anatumiza mithenga kwa anthu a ku Jabezi Gileadi, nanena nao, Mudalitsike ndi Yehova inu, popeza munacitira cokoma ici mbuye wanu Sauli, ndi kumuika.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:5 nkhani