Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 2:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo zitatha izi Davide anafunsira kwa Yehova nati, Kodi ndikwere kunka m'mudzi wina wa Yuda? Ndipo Yehova ananena naye, Kwera. Davide nanena naye, Ndikwere kuti? Ndipo anati, Ku Hebroni.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:1 nkhani