Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Samueli 2:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Comweco Davide anakwera kunka kumeneko pamodzi ndi akazi ace awiri, ndiwo Ahingamu Mjezreeli, ndi Abigayeli mkazi wa Nabala wa ku Karimeli.

Werengani mutu wathunthu 2 Samueli 2

Onani 2 Samueli 2:2 nkhani