Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 25:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mnyamata wina anauza Abigayeli, mkazi wa Nabala, kuti, Onani, Davide anatumiza mithenga akucokera kucipululu kulankhula mbuye wathu; koma iye anawakalipira.

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 25

Onani 1 Samueli 25:14 nkhani