Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Samueli 10:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamene anafika kucitunda kuja, onani, gulu la aneneri linakomana naye; ndi Mzimu wa Mulungu unamgwera mwamphamvu, iye nanenera pakati pao,

Werengani mutu wathunthu 1 Samueli 10

Onani 1 Samueli 10:10 nkhani