Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Mafumu 8:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mfumu Solomo ndi msonkhano wonse wa Israyeli wosonkhana kwa iye anali naye kulikasa, naphera nkhosa ndi ng'ombe za nsembe zosawerengeka ndi zosadziwika, cifukwa ca unyinji wao.

Werengani mutu wathunthu 1 Mafumu 8

Onani 1 Mafumu 8:5 nkhani