Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 9:44-48 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

44. ]

45. Ndipo ngati phazi lako likulakwitsa, ulidule; kulowa iwe m'moyo wopunduka mwendo, kuli kwabwino koposa ndi kukhala ndi mapazi ako awiri ndi kuponyedwa m'gehena.[

46. ]

47. Ndipo ngati diso lako likulakwitsa ulikolowole; kulowa iwe m'Ufumu wa Mulungu ndi diso limodzi kuli kwabwino koposa ndi kukhala ndi maso awiri ndi kuponyedwa m'gehena;

48. kumeneko mphutsi yao siikufa, ndi mota suzimidwa.

Werengani mutu wathunthu Marko 9