Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 9:43 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ngati dzanja lako likulakwitsa iwe, ulidule: nkwabwino kwa iwe kulowa m'moyo wopunduka dzanja, koposa kukhala ndi manja ako awiri ndi kulowa m'gehena, m'moto wosazima.[

Werengani mutu wathunthu Marko 9

Onani Marko 9:43 nkhani