Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Marko 6:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pofika dzuwa la Sabata, anayamba kuphunzitsa m'sunagoge; ndipo ambiri anamva Iye, nazizwa, nanena, Uyu adazitenga kuti izi? Nzeru yopatsidwa kwa munthuyu njotani, ndi zamphamvu zotere zocitidwa ndi manja ace?

Werengani mutu wathunthu Marko 6

Onani Marko 6:2 nkhani