Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 9:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma unyinji wa anthu, pamene anadziwa, anamtsata Iye; ndipo iye anawalandira, nalankhula nao za Ufumu wa Mulungu, naciritsa amene anasowa kuciritsidwa.

Werengani mutu wathunthu Luka 9

Onani Luka 9:11 nkhani