Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 4:7-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Cifukwa cace ngati Inu mudzagwadira pamaso panga, wonsewo udzakhala wanu.

8. Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwalembedwa, kuti,Ambuye Mulungu wako uzimgwadira,Ndipo iye yekha yekha uzimtumikira,

9. Ndipo anamtsogolera iye ku Yerusalemu, namuika iye pamwamba pa cimbudzi ca Kacisiyo, nati kwa iye, Ngati muli Mwana wa Mulungu, tadzigwetsani nokha pansi;

10. pakuti kwalembedwa, kuti,Adzalamulira angelo ace za, iwe, kuti akucinjirize,

11. Ndipo,Pa manja ao adzakunyamula iwe,Kuti ungagunde konse phazi lako pamwala,

12. Ndipo Yesu anayankha, nati kwa iye, Kwanenedwa,Usamuyese Ambuye Mulungu wako,

Werengani mutu wathunthu Luka 4