Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 4:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mdierekezi anati kwa iye, Ine ndidzapatsa Inu ulamuliro wonse umenewu ndi ulemerero wao: cifukwa unaperekedwa kwa ine; ndipo ndiupatsa kwa iye amene ndifuna.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:6 nkhani