Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 4:41 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi ziwanda zomwe zinaturuka mwa ambiri, ndi kupfuula, kuti, Inu ndinu Mwana wa Mulungu. Ndipo iye anazidzudzula, wosazilola kulankhula, cifukwa zinamdziwa kuti iye ndiye Kristu.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:41 nkhani