Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 4:32-35 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

32. cifukwa mau ace anali ndi ulamuliro.

33. Ndipo munali m'sunagoge munthu, wokhala naco ciwanda conyansa; napfuula ndi mau olimba, kuti,

34. Ha! tiri ndi ciani ndi Inu, Yesu wa ku N azarete? kodi munadza kutiononga ife? ndikudziwani Inu muli yani, ndinu Woyera wace wa Mulungu.

35. Ndipo Yesu anamdzudzula iye, nanena, Tonthola, nuturuke mwa iye. Ndipo ciwandaco m'mene cinamgwetsa iye pakati, cinaturuka mwa iye cosampweteka konse.

Werengani mutu wathunthu Luka 4