Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 4:36 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anthu onse anadabwa, nalankhulana wina ndi mnzace, nanena, Mau amenewa ali otani? cifukwa ndi ulamuliro ndi mphamvu angolamulira mizimu yonyansa, ndipo ingoturuka.

Werengani mutu wathunthu Luka 4

Onani Luka 4:36 nkhani