Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 5:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo mmodzi wa akuru ananena ndi ine, Usalire: taona, Mkango wocokera m'pfuko la Yuda, Muzu wa Davide, walakika kutsegula buku ndi zizindikilo zace zisanu ndi ziwiri.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 5

Onani Cibvumbulutso 5:5 nkhani