Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 5:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinaona pakati pa mpando wacifumu ndi zamoyo zinai, ndi pakati pa akuru, Mwanawankhosa ali ciriri ngati waphedwa; wokhala nazo nyanga zisanu ndi ziwiri, ndi maso asanu ndi awiri, ndiyo mizimu isanu ndi iwiri ya Mulungu, yotumidwa ilowe m'dziko lonse.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 5

Onani Cibvumbulutso 5:6 nkhani