Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 22:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo sipadzakhalanso temberero liri lonse; ndipo mpando wacifumu wa Mulungu ndi wa Mwanawankhosa udzakhala momwemo; ndipo akapolo ace adzamtumikira iye,

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 22

Onani Cibvumbulutso 22:3 nkhani