Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 11:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo amitundu anakwiya, ndipo unadza mkwiyo wanu, ndi nthawi ya akufa yakuti aweruzidwe, ndi yakupereka mphotho akapolo anu aneneriwo, ndi oyera mtima, ndi iwo akuopa dzina lanu, ang'ono ndi akuru; ndi kuononga iwo akuononga dziko.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 11

Onani Cibvumbulutso 11:18 nkhani