9. Ndipo ciani tsono? kodi tiposa ife? Iai ndithu; pakuti tidawaneneza kale Ayuda ndi Ahelene omwe, kuti onsewa agwidwa ndi ucimo;
10. monga kwalembedwa,Palibe mmodzi wolungama, inde palibe mmodzi;
11. Palibe mmodzi wakudziwitsa, Palibe mmodzi wakuloodola Mulungu;
12. Onsewa apatuka, pamodzi akhala opanda pace;Palibe mmodzi wakucita zabwino, inde, palibe mmodzi ndithu.