Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 5:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kunali, pokhala Yoswa ku Yeriko, anakweza maso ace, napenya, ndipo taona, panaima muthu pandunji pace ndi lupanga lace losolola m'dzanja lace; namuka Yoswa kuli iye, nati iye, Ubvomerezana ndi ife kapena ndi aelani athu?

Werengani mutu wathunthu Yoswa 5

Onani Yoswa 5:13 nkhani