Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 23:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kudzakhala kuti monga zakugwerani zokoma zonse anakunenerani Yehova Mulungu wanu, momwemo Yehova adzakutengerani zoipa zonse mpaka atakuonongani kukucotsani m'dziko lokoma ili anakupatsani Yehova Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 23

Onani Yoswa 23:15 nkhani