Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 23:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

dziwani ndithu kuti Yehova Mulungu wanu sadzalandanso dziko la amitundu awa kuwacotsa pamaso panu; koma adzakhala kwa inu deka ndi msampha ndi mkwapulo m'nthiti mwanu, ndi minga m'maso mwanu, mpaka mudzatayika m'dziko lokoma ili anakupatsani Yehova Mulungu wanu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 23

Onani Yoswa 23:13 nkhani