Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 22:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ana a Rubeni, ndi ana a Gadi, ndi pfuko la Manase logawika pakati anabwerera, nacoka kwa ana a Israyeli ku Silo, ndiwo wa m'dziko la Kanani kumka ku dziko la Gileadi, ku dziko lao lao, limene anakhala eni ace, monga mwa lamulo la Yehova, mwa dzanja la Mose.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:9 nkhani