Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 22:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

nanena nao ndi kuti, Bwererani naco cuma cambiri ku mahema anu, ndi zoweta zambirimbiri, ndi siliva, ndi golidi, ndi mkuwa, ndi citsulo, ndi maraya ambirimbiri; mugawane nao abale anu zofunkha kwa adani anu.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 22

Onani Yoswa 22:8 nkhani