Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 19:38-46 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

38. ndi Ironi, ndi Migidala-eli, Horemu, ndi Betianati, ndi Beti-semesi; midzi khumi ndi isanu ndi inai, ndi miraga yao.

39. Ici ndi colowa ca pfuko la ana a Nafitali, monga mwa mabanja ao, midzi ndi miraga yao.

40. Maere acisanu ndi ciwiri anaturukira pfuko la ana a Dani, monga mwa mabanja ao.

41. Ndipo malire a colowa cao anali Zora, ndi Esitaoli ndi Iri-semesi;

42. Saalabini, ndi Aijaloni ndi ltila;

43. ndi Eloni ndi Timna ndi Ekroni;

44. ndi Eliteke, ndi Gibetoni, ndi Baalati;

45. ndi Yehudi, ndi Bene-beraki, ndi Gatirimoni;

46. ndi Me-jarikoni, ndi Rakoni, ndi malire pandunji pajapo.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 19