Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 16:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo malire a ana a Efraimu, monga mwa mabanja ao, ndiwo: malire a colowa cao kum'mawa ndiwo Atarotu-Adara, mpaka Betihoroni wa kumtunda;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 16

Onani Yoswa 16:5 nkhani