Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 16:4-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Motero ana a Yosefe, Manase ndi Efraimu analandira colowa cao,

5. Ndipo malire a ana a Efraimu, monga mwa mabanja ao, ndiwo: malire a colowa cao kum'mawa ndiwo Atarotu-Adara, mpaka Betihoroni wa kumtunda;

6. naturuka malire kumadzulo ku Mikametatu kumpoto; nazungulira malire kum'mawa kumka ku Taanatu-silo, naupitirira kum'mawa kwace kwa Yanoa:

Werengani mutu wathunthu Yoswa 16