Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 15:60-63 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

60. Kiriyata-Baala, ndiwo KiriyatiYearimu ndi Raba; midzi iwiri pamodzi ndi miraga yao.

61. M'cipululu, Beti-araba, Midini, ndi Sekaka;

62. ndi Nibisani, ndi Mudzi wa Mcere, ndi En-gedi; midzi isanu ndi umodzi pamodzi ndi miraga yao.

63. Koma ana a Yuda sanakhoza kuingitsa Ayebusi, nzika za Yerusalemu: m'mwemo Ayebusi anakhala pamodzi ndi ana a Yuda, ku Yerusalemu, mpaka lero lino.

Werengani mutu wathunthu Yoswa 15