Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yoswa 13:23-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Ndipo malire a ana a Rubeni ndiwo Yordano ndi malire ace. Ndico colandira ca ana a Rubeni monga mwa mabanja ao, midzi yace ndi miraga yace.

24. Ndipo Mose anapatsira pfuko la Gadi, ana a Gadi, monga mwa mabanja ao.

25. Ndipo malire ao ndiwo Yazeri, ndi midzi yonse ya Gileadi, ndi dziko la ana a Amoni logawika pakati, mpaka ku Aroeri, wokhala cakuno ca Raba;

26. ndi kuyambira Hesiboni mpaka Ramati-Mizipe, ndi Betonimu; ndi kuyambira Mahanaimu mpaka malire a Dibiri;

Werengani mutu wathunthu Yoswa 13