Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 66:18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti Ine ndidziwa nchito zao ndi maganizo ao; nthawi ikudza yakudzasonkhanitsa Ine a mitundu yonse ndi zinenedwe zonse, ndipo adzafika nadzaona ulemerero wanga.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 66

Onani Yesaya 66:18 nkhani