Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 66:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iwo amene adzipatulitsa nadziyeretsa, kuti amuke kuminda tsatane tsatane, ndi kudya nyama ya nkhumba, ndi conyansa, ndi mbewa, adzathedwa pamodzi, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 66

Onani Yesaya 66:17 nkhani