Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 60:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Zoweta za Kedara zidzasonkhana kwa iwe, nkhosa zamphongo za Nebaioti zidzakutumikira; izo zidzafika ndi kulandiridwa pa guwa langa la nsembe; ndipo ndidzakometsa nyumba ya ulemerero wanga.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 60

Onani Yesaya 60:7 nkhani