Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 57:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndi kumbuyo kwa zitseko ndi mphuthu waimiritsa cikumbutso cako, pakuti wadzionetsa wekha kwa wina, wosati kwa Ine; ndipo wakwerako, wakuza mphasa yako, ndi kupangana nao pangano; unakonda mphasa yao kumene unaiona.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 57

Onani Yesaya 57:8 nkhani