Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 44:7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndani adzaitana monga Ine, ndi kulalikira ici ndi kundilongosolera ici, cikhazikitsire Ine anthu akale? milunguyo iwadziwitse zomwe zirinkudza, ndi za m'tsogolo.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 44

Onani Yesaya 44:7 nkhani