Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Yesaya 41:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Wosauka ndi wosowa afuna madzi, ndipo palibe, ndi lilume lao lilephera, cifukwa ca ludzu; Ine Yehova ndidzawayankha, Ine Mulungu wa Israyeli sindidzawasiya.

Werengani mutu wathunthu Yesaya 41

Onani Yesaya 41:17 nkhani